Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 27:36 - Buku Lopatulika

36 nakhala iwo pansi, namdikira kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 nakhala iwo pansi, namdikira kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Kenaka adakhala pansi namamlonda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Ndipo anakhala pansi namulonda Iye.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:36
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anaika pamwamba pamutu pake mlandu wake wolembedwa: UYU NDI YESU MFUMU YA AYUDA.


Ndipo anali naye akudikira Yesu, anaona chivomezi, ndi zinthu zimene zinachitidwa, anaopa kwambiri, nanena, Indedi Uyu ndiye Mwana wa Mulungu.


Ndipo pamene kenturiyo, woimirirapo popenyana ndi Iye, anaona kuti anapereka mzimu kotero, anati, Zoonadi, munthu uyu anali Mwana wa Mulungu.


Ndipo Pilato anazizwa ngati adamwaliradi; naitana kenturiyo, namfunsa ngati adamwalira kale.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa