Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 27:35 - Buku Lopatulika

35 Ndipo pamene anampachika Iye, anagawana zovala zake ndi kulota maere:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Ndipo pamene anampachika Iye, anagawana zovala zake ndi kulota maere:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Atampachika pa mtanda, adagaŵana zovala zake pakuchita maere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Atamupachika Iye, anagawana zovala zake pochita maere.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:35
10 Mawu Ofanana  

Pakuti andizinga agalu, msonkhano wa oipa wanditsekereza; andiboola m'manja anga ndi m'mapazi anga.


Agawana zovala zanga, nachita maere pa malaya anga.


Ndipo Yesu ananena, Atate, muwakhululukire iwo, pakuti sadziwa chimene achita. Ndipo anagawana zovala zake, poyesa maere.


Ndipo pamene adanena ichi, anaonetsa iwo manja ake ndi nthiti zake. Pamenepo ophunzira anakondwera pakuona Ambuye.


Chifukwa chake ophunzira ena ananena naye, Tamuona Ambuye. Koma iye anati kwa iwo, Ndikapanda kuona m'manja ake chizindikiro cha misomaliyo, ndi kuika chala changa m'chizindikiro cha misomaliyo, ndi kuika dzanja langa kunthiti yake; sindidzakhulupirira.


Pomwepo ananena kwa Tomasi, Bwera nacho chala chako kuno, nuone manja anga, ndipo bwera nalo dzanja lako, nuliike kunthiti yanga, ndipo usakhale wosakhulupirira, koma wokhulupirira.


ameneyo, woperekedwa ndi uphungu woikidwa ndi kudziwiratu kwa Mulungu, inu mwampachika ndi kumupha ndi manja a anthu osaweruzika;


zindikirani inu nonse, ndi anthu onse a Israele, kuti m'dzina la Yesu Khristu Mnazarayo, amene inu munampachika pamtanda, amene Mulungu anamuukitsa kwa akufa, mwa Iyeyu munthuyu aimirirapo pamaso panu, wamoyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa