Mateyu 27:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo pamene anampachika Iye, anagawana zovala zake ndi kulota maere: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo pamene anampachika Iye, anagawana zovala zake ndi kulota maere: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Atampachika pa mtanda, adagaŵana zovala zake pakuchita maere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Atamupachika Iye, anagawana zovala zake pochita maere. Onani mutuwo |