Mateyu 27:2 - Buku Lopatulika2 ndipo anammanga Iye, namuka naye, nampereka Iye kwa Pilato kazembeyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndipo anammanga Iye, namuka naye, nampereka Iye kwa Pilato kazembeyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adammanga, napita naye kwa Pilato, bwanamkubwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Anamumanga, napita naye kukamupereka kwa bwanamkubwa Pilato. Onani mutuwo |