Mateyu 27:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo sanayankhe Iye, ngakhale mau amodzi, kotero kuti kazembe anazizwa ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo sanayankhe Iye, ngakhale mau amodzi, kotero kuti kazembe anazizwa ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma Yesu sadamuyankhe kanthu, kotero kuti bwanamkubwa uja adadabwa kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma Yesu sanayankhe ngakhale mawu amodzi mpaka bwanamkubwa anadabwa kwambiri. Onani mutuwo |