Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 27:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo pa chikondwerero kazembe adazolowera kumasulira anthu mmodzi wandende, amene iwo anafuna.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo pa chikondwerero kazembe adazolowera kumasulira anthu mmodzi wandende, amene iwo anafuna.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Pa nthaŵi ya chikondwerero cha Paska, bwanamkubwa ankaŵamasulira anthu mkaidi mmodzi, yemwe iwo ankafuna.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Pa nthawiyi chinali chizolowezi cha bwanamkubwa kuti pachikondwerero cha Paska amamasula wamʼndende wosankhidwa ndi anthu.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:15
11 Mawu Ofanana  

Koma ananena iwo, pa nthawi ya chikondwerero iai, kuti pasakhale phokoso la anthu.


Ndipo pa nthawi yomweyo anali ndi wandende wodziwika, dzina lake Barabasi.


Chifukwa chake ndidzamkwapula ndi kummasula Iye.


Koma iwo onse pamodzi anafuula, nati, Chotsani munthu uyu, mutimasulire Barabasi;


koma Petro anaima kukhomo kunja. Chifukwa chake wophunzira winayo amene anadziwika kwa mkulu wa ansembe, anatuluka nalankhula ndi wapakhomo, nalowetsa Petro.


Ndipo pamenepo anampereka Iye kwa iwo kuti ampachike. Pamenepo anatenga Yesu;


Koma zitapita zaka ziwiri Porkio Fesito analowa m'malo a Felikisi; ndipo Felikisi pofuna kukonda Ayuda anamsiya Paulo m'nsinga.


Koma Fesito pofuna kuyesedwa wachisomo ndi Ayuda, anayankha kwa Paulo, nati, Kodi ufuna kukwera kunka ku Yerusalemu, ndi kuweruzidwa ndi ine pomwepo kunena za zinthu izi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa