Mateyu 27:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo pa chikondwerero kazembe adazolowera kumasulira anthu mmodzi wandende, amene iwo anafuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo pa chikondwerero kazembe adazolowera kumasulira anthu mmodzi wandende, amene iwo anafuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Pa nthaŵi ya chikondwerero cha Paska, bwanamkubwa ankaŵamasulira anthu mkaidi mmodzi, yemwe iwo ankafuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Pa nthawiyi chinali chizolowezi cha bwanamkubwa kuti pachikondwerero cha Paska amamasula wamʼndende wosankhidwa ndi anthu. Onani mutuwo |