Mateyu 26:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti mafuta awa akadagulitsa ndalama zambiri, ndi kuzipatsa anthu aumphawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti mafuta awa akadagulitsa ndalama zambiri, ndi kuzipatsa anthu aumphawi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndithu mafuta ameneŵa akadatha kuŵagulitsa pa mtengo waukulu zedi, kenaka ndalama zake nkukapatsa anthu osauka.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mafuta amenewa akanatha kugulitsidwa pa mtengo waukulu, ndipo ndalama zake zikanaperekedwa kwa osauka.” Onani mutuwo |