Mateyu 26:70 - Buku Lopatulika70 Koma iye anakana pamaso pa anthu onse, kuti, Chimene unena sindichidziwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201470 Koma iye anakana pamaso pa anthu onse, kuti, Chimene unena sindichidziwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa70 Koma iye adakana pamaso pa anthu onse, adati, “Sindikuzidziŵa zimenezo ine.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero70 Koma iye anakana pamaso pawo nati, “Sindikudziwa chimene ukunena.” Onani mutuwo |