Mateyu 26:69 - Buku Lopatulika69 Ndipo Petro adakhala pabwalo: ndipo mdzakazi anadza kwa iye, nanena, Iwenso unali ndi Yesu wa ku Galileya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201469 Ndipo Petro adakhala pabwalo: ndipo mdzakazi anadza kwa iye, nanena, Iwenso unali ndi Yesu wa ku Galileya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa69 Petro adaakhala kunja m'bwalo la nyumba ija. Mtsikana wina wantchito adabwera namuuza kuti, “Inunsotu munali ndi Yesu wa ku Nazareteyu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero69 Tsopano Petro anakhala ku bwalo la nyumbayo, ndipo mtsikana wantchito anabwera kwa iye nati, “Iwenso unali ndi Yesu wa ku Galileya.” Onani mutuwo |