Mateyu 26:61 - Buku Lopatulika61 nati, Uyu ananena kuti, Ndikhoza kupasula Kachisi wa Mulunguyu, ndi kummanganso masiku atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201461 nati, Uyu ananena kuti, Ndikhoza kupasula Kachisi wa Mulunguyu, ndi kummanganso masiku atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa61 Adati, “Munthu uyu ankati, ‘Ine ndingathe kupasula Nyumba ya Mulungu nkuimanganso pa masiku atatu.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero61 Ndipo zinati, “Munthu uyu anati, ‘Ndikhoza kupasula Nyumba ya Mulungu ndi kuyimanganso mʼmasiku atatu.’ ” Onani mutuwo |