Mateyu 26:60 - Buku Lopatulika60 koma sanaupeze zingakhale mboni zonama zambiri zinadza. Koma pambuyo pake anadza awiri, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201460 koma sanaupeze zingakhale mboni zonama zambiri zinadza. Koma pambuyo pake anadza awiri, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa60 Koma sadaupeze ngakhale padaabwera mboni zambiri zabodza. Potsiriza padabwera anthu aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero60 Koma sanathe kupeza uliwonse, angakhale kuti mboni zambiri zabodza zinapezeka. Pomalizira mboni ziwiri zinabwera patsogolo. Onani mutuwo |