Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 26:60 - Buku Lopatulika

60 koma sanaupeze zingakhale mboni zonama zambiri zinadza. Koma pambuyo pake anadza awiri,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

60 koma sanaupeze zingakhale mboni zonama zambiri zinadza. Koma pambuyo pake anadza awiri,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

60 Koma sadaupeze ngakhale padaabwera mboni zambiri zabodza. Potsiriza padabwera anthu aŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

60 Koma sanathe kupeza uliwonse, angakhale kuti mboni zambiri zabodza zinapezeka. Pomalizira mboni ziwiri zinabwera patsogolo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 26:60
7 Mawu Ofanana  

Musandipereke ku chifuniro cha akundisautsa, chifukwa zinandiukira mboni zonama ndi iwo akupumira zachiwawa.


Mboni za chiwawa ziuka, zindifunsa zosadziwa ine.


Mboni imodzi isamaukira munthu pa mphulupulu iliyonse, kapena tchimo lililonse adalichimwa; pakamwa pa mboni ziwiri, kapena pakamwa pa mboni zitatu mlandu utsimikizike.


mau olama osatsutsika; kuti iye wakutsutsana achite manyazi, posakhala nako kanthu koipa kakutinenera ife.


ndi kukhala nacho chikumbumtima chabwino, kuti umo akunenerani, iwo akunenera konama mayendedwe anu abwino mu Khristu akachitidwe manyazi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa