Mateyu 26:33 - Buku Lopatulika33 Koma Petro ananena kwa Iye, Ngakhale onse adzakhumudwa chifukwa cha Inu, ine sindidzakhumudwa nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Koma Petro ananena kwa Iye, Ngakhale onse adzakhumudwa chifukwa cha Inu, ine sindidzakhumudwa nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Petro adati, “Ngakhale onse akhumudwe nkukusiyani, ine ndekha ai.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Petro anayankha nati, “Ngakhale onsewa atakuthawani, ine ndekha ayi.” Onani mutuwo |