Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 26:33 - Buku Lopatulika

33 Koma Petro ananena kwa Iye, Ngakhale onse adzakhumudwa chifukwa cha Inu, ine sindidzakhumudwa nthawi zonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Koma Petro ananena kwa Iye, Ngakhale onse adzakhumudwa chifukwa cha Inu, ine sindidzakhumudwa nthawi zonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Petro adati, “Ngakhale onse akhumudwe nkukusiyani, ine ndekha ai.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Petro anayankha nati, “Ngakhale onsewa atakuthawani, ine ndekha ayi.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 26:33
15 Mawu Ofanana  

M'mayendedwe anga ndasunga mabande anu, mapazi anga sanaterereke.


Anthu ambiri abukitsa yense kukoma mtima kwake; koma ndani angapeze munthu wokhulupirika?


Mtima ndiwo wonyenga koposa, ndi wosachiritsika, ndani angathe kuudziwa?


Koma nditauka ndidzatsogolera inu ku Galileya.


Yesu anati kwa iye, Indetu ndinena kwa iwe, kuti usiku uno, tambala asanalire, udzandikana Ine katatu.


Koma Petro ananena naye, Angakhale adzakhumudwa onse, komatu ine iai.


Ndipo anati kwa Iye, Ambuye, ndilipo ndikapite ndi Inu kundende ndi kuimfa.


Ndipo pamene atafisula Yesu ananena kwa Simoni Petro, Simoni mwana wa Yona, kodi undikonda Ine koposa awa? Ananena ndi Iye, Inde, Ambuye; mudziwa kuti ndikukondani Inu. Ananena naye, Dyetsa anaankhosa anga.


M'chikondano cha anzanu wina ndi mnzake mukondane ndi chikondi chenicheni; mutsogolerane ndi kuchitira wina mnzake ulemu;


musachite kanthu monga mwa chotetana, kapena monga mwa ulemerero wopanda pake, komatu ndi kudzichepetsa mtima, yense ayese anzake omposa iye mwini;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa