Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 26:32 - Buku Lopatulika

32 Koma nditauka ndidzatsogolera inu ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Koma nditauka ndidzatsogolera inu ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Koma ndikadzauka kwa akufa, ndidzatsogola ndine kupita ku Galileya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Koma ndikadzauka, ndidzatsogola kupita ku Galileya.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 26:32
13 Mawu Ofanana  

Kuyambira pamenepo Yesu anayamba kuwalangiza ophunzira ake, kuti kuyenera Iye amuke ku Yerusalemu, kukazunzidwa zambiri ndi akulu, ndi ansembe aakulu, ndi alembi; ndi kukaphedwa, ndi tsiku lachitatu kuuka kwa akufa.


nadzampereka kwa anthu akunja kuti amnyoze ndi kumkwapula, ndi kumpachika; ndipo Iye adzaukitsidwa tsiku lachitatu.


Koma Petro ananena kwa Iye, Ngakhale onse adzakhumudwa chifukwa cha Inu, ine sindidzakhumudwa nthawi zonse.


Pomwepo Yesu ananena kwa iwo, Musaope; pitani, kauzeni abale anga kuti amuke ku Galileya, ndipo adzandiona Ine kumeneko.


Koma ophunzira khumi ndi mmodziwo anamuka ku Galileya, kuphiri kumene Yesu anawapangira.


Komatu nditadzauka ndidzatsogolera inu ku Galileya.


Koma mukani, uzani ophunzira ake, ndi Petro, kuti akutsogolerani inu ku Galileya; kumeneko mudzamuona Iye, monga ananena ndi inu.


pomwepo anaoneka pa nthawi imodzi kwa abale oposa mazana asanu, amene ochuluka a iwo akhala kufikira tsopano, koma ena agona;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa