Mateyu 26:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo Iye anayankha nati, Iye amene asunsa pamodzi ndi Ine dzanja lake m'mbale, yemweyu adzandipereka Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo Iye anayankha nati, Iye amene asunsa pamodzi ndi Ine dzanja lake m'mbale, yemweyu adzandipereka Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Yesu adaŵayankha kuti, “Yemwe wasunsa mkate m'mbalemu pamodzi ndi Ine, ameneyo ndiye andipereke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Yesu anayankha nati, “Iye amene akusunsa mʼmbale pamodzi ndi Ine, yemweyo adzandipereka. Onani mutuwo |