Mateyu 26:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo iwo anagwidwa ndi chisoni chachikulu, nayamba kunena kwa Iye mmodzimmodzi, Kodi ndine, Ambuye? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo iwo anagwidwa ndi chisoni chachikulu, nayamba kunena kwa Iye mmodzimmodzi, Kodi ndine, Ambuye? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ophunzirawo adamva chisoni kwambiri, nayamba mmodzimmodzi kumufunsa kuti, “Monga nkukhala ine, Ambuye?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Iwo anamva chisoni kwambiri ndipo anayamba kuyankhulana naye mmodzimmodzi nati, “Kodi nʼkukhala ine Ambuye?” Onani mutuwo |