Mateyu 26:21 - Buku Lopatulika21 ndipo m'mene analinkudya, Iye anati, Indetu ndinena kwa inu, mmodzi wa inu adzandipereka Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 ndipo m'mene analinkudya, Iye anati, Indetu ndinena kwa inu, mmodzi wa inu adzandipereka Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Iwowo alikudya, Yesu adaŵauza kuti, “Ndithu ndikunenetsa kuti wina mwa inu andipereka kwa adani anga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Akudya, Iye anati, “Zoonadi, ndikuwuzani kuti mmodzi wa inu adzandipereka.” Onani mutuwo |