Mateyu 26:11 - Buku Lopatulika11 Pakuti nthawi zonse muli nao aumphawi pamodzi nanu; koma simuli ndi Ine nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pakuti nthawi zonse muli nao aumphawi pamodzi nanu; koma simuli ndi Ine nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Anthu osauka muli nawo nthaŵi zonse, koma Ine simudzakhala nane nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Osauka mudzakhala nawo nthawi zonse, koma simudzakhala ndi Ine nthawi zonse. Onani mutuwo |