Mateyu 26:12 - Buku Lopatulika12 Pakuti mkaziyo, m'mene anathira mafuta awa pathupi panga, wandichitiratu ichi pa kuikidwa kwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pakuti mkaziyo, m'mene anathira mafuta awa pathupi panga, wandichitiratu ichi pa kuikidwa kwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Iyeyu wathira mafuta ameneŵa pa thupi langa kuti alidzozeretu lisanaikidwe m'manda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Pamene wathira mafuta onunkhirawa pa thupi langa, wachita izi kukonzekera kuyikidwa kwanga mʼmanda. Onani mutuwo |