Mateyu 25:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo opusa anati kwa ochenjera, Tipatseniko ena a mafuta anu; chifukwa nyali zathu zilikuzima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo opusa anati kwa ochenjera, Tipatseniko ena a mafuta anu; chifukwa nyali zathu zilikuzima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Opusa aja adapempha ochenjera aja kuti, ‘Tipatseniko mafuta, onani nyale zathu zikuzima.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Opusawo anati kwa ochenjerawo, ‘Tipatseniko mafuta anu; nyale zathu zikuzima.’ Onani mutuwo |