Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 25:7 - Buku Lopatulika

7 Pomwepo anauka anamwali onse amenewo, nakonza nyali zao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Pomwepo anauka anamwali onse amenewo, nakonza nyali zao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Anamwali khumi aja adadzuka, nkuyamba kukonza nyale zao zija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 “Pamenepo anamwali onse anadzuka nayatsa nyale zawo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 25:7
8 Mawu Ofanana  

Pomwepo Ufumu wa Kumwamba udzafanizidwa ndi anamwali khumi, amene anatenga nyali zao, natuluka kukakomana ndi mkwati.


Koma pakati pa usiku panali kufuula, Onani, mkwati! Tulukani kukakomana naye.


Ndipo opusa anati kwa ochenjera, Tipatseniko ena a mafuta anu; chifukwa nyali zathu zilikuzima.


Khalani odzimangira m'chuuno, ndipo nyali zanu zikhale zoyaka;


Momwemo, okondedwa, popeza muyembekeza izi, chitani changu kuti mupezedwe ndi Iye mumtendere, opanda banga ndi opanda chilema.


Khala wodikira, ndipo limbitsa zotsalira zimene zinafuna kufa; pakuti sindinapeze ntchito zako zakufikira pamaso pa Mulungu wanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa