Mateyu 25:6 - Buku Lopatulika6 Koma pakati pa usiku panali kufuula, Onani, mkwati! Tulukani kukakomana naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma pakati pa usiku panali kufuula, Onani, mkwati! Tulukani kukakomana naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Tsono pakati pa usiku kudamveka kufuula kuti, ‘Mkwati akubwera! Tulukani, kamchingamireni!’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Pakati pa usiku kunamveka kufuwula kuti, ‘Onani Mkwati! Tulukani kuti mukakumane naye!’ Onani mutuwo |