Mateyu 25:12 - Buku Lopatulika12 Koma iye anayankha nati, Indetu ndinena kwa inu, sindikudziwani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma iye anayankha nati, Indetu ndinena kwa inu, sindikudziwani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Koma mkwatiyo adati, ‘Pepani, sindikukudziŵani!’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Koma iye anayankha kuti, ‘Zoonadi, ine ndikuwuzani kuti sindikukudziwani.’ Onani mutuwo |