Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 25:12 - Buku Lopatulika

12 Koma iye anayankha nati, Indetu ndinena kwa inu, sindikudziwani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Koma iye anayankha nati, Indetu ndinena kwa inu, sindikudziwani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Koma mkwatiyo adati, ‘Pepani, sindikukudziŵani!’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 “Koma iye anayankha kuti, ‘Zoonadi, ine ndikuwuzani kuti sindikukudziwani.’

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 25:12
12 Mawu Ofanana  

Pakuti Yehova adziwa mayendedwe a olungama; koma mayendedwe a oipa adzatayika.


Opusa sadzakhazikika pamaso panu, mudana nao onse akuchita zopanda pake.


Inu wa maso osalakwa, osapenya choipa, osakhoza kupenyerera chovuta, mupenyereranji iwo akuchita mochenjerera, ndi kukhala chete pamene woipa ammeza munthu wolungama woposa iye mwini;


Koma pambuyo pake anadzanso anamwali enawo, nati, Mbuye, mbuye, mutitsegulire ife.


Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake, kapena nthawi yake.


Pamene atauka mwini nyumba natseka pakhomo, ndipo inu mudzayamba kuima pabwalo, ndi kugogoda pachitseko, ndi kunena, Ambuye titsegulireni ife; ndipo Iye adzayankha nadzati ndi inu, Sindidziwa inu kumene muchokerako;


Nkhosa zanga zimva mau anga, ndipo Ine ndizizindikira, ndipo zinditsata Ine.


Tidziwa kuti Mulungu samvera ochimwa. Koma ngati munthu aliyense akhala wopembedza Mulungu nachita chifuniro chake, amvera ameneyo.


Koma ngati wina akonda Mulungu, yemweyu adziwika ndi Iye.


koma tsopano, podziwa Mulungu inu, koma makamaka podziwika ndi Mulungu, mubwereranso bwanji kutsata miyambo yofooka ndi yaumphawi, imene mufuna kubwerezanso kuichitira ukapolo?


Koma ndithu maziko a Mulungu aimika pokhazikika, ndi kukhala nacho chizindikiro ichi, Ambuye azindikira iwo amene ali ake; ndipo, Adzipatule kwa chosalungama yense wakutchula dzina la Ambuye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa