Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 25:13 - Buku Lopatulika

13 Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake, kapena nthawi yake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake, kapena nthawi yake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Pomaliza Yesu adati, “Ndiyetu inu, muzikhala maso, poti simudziŵa tsiku lake kapena nthaŵi yake.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 “Choncho khalani odikira, popeza simudziwa tsiku kapena nthawi.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 25:13
12 Mawu Ofanana  

mbuye wa kapoloyo adzafika tsiku losamuyembekeza iye, ndi nthawi yosadziwa iye,


Koma iye anayankha nati, Indetu ndinena kwa inu, sindikudziwani.


Koma inu dikirani nyengo zonse, ndi kupemphera, kuti mukalimbike kupulumuka zonse zimene zidzachitika, ndi kuimirira pamaso pa Mwana wa Munthu.


Chifukwa chake dikirani, nimukumbukire kuti zaka zitatu sindinaleke usiku ndi usana kuchenjeza yense wa inu ndi misozi.


Dikirani, chilimikani m'chikhulupiriro, dzikhalitseni amuna, limbikani.


chifukwa chake tsono tisagone monga otsalawo, komatu tidikire, ndipo tisaledzere.


Koma iwe, khala maso m'zonse, imva zowawa, chita ntchito ya mlaliki wa Uthenga Wabwino, kwaniritsa utumiki wako.


Koma chitsiriziro cha zinthu zonse chili pafupi; chifukwa chake khalani anzeru, ndipo dikirani m'mapemphero;


Khalani odzisungira, dikirani; mdani wanu mdierekezi, monga mkango wobuma, ayendayenda ndi kufunafuna wina akamlikwire:


(Taonani, ndidza ngati mbala. Wodala iye amene adikira, nasunga zovala zake, kuti angayende wausiwa, nangapenye anthu usiwa wake.)


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa