Mateyu 25:13 - Buku Lopatulika13 Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake, kapena nthawi yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake, kapena nthawi yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Pomaliza Yesu adati, “Ndiyetu inu, muzikhala maso, poti simudziŵa tsiku lake kapena nthaŵi yake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 “Choncho khalani odikira, popeza simudziwa tsiku kapena nthawi.” Onani mutuwo |