Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 25:11 - Buku Lopatulika

11 Koma pambuyo pake anadzanso anamwali enawo, nati, Mbuye, mbuye, mutitsegulire ife.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Koma pambuyo pake anadzanso anamwali enawo, nati, Mbuye, Mbuye, mutitsegulire ife.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 “Kenaka m'mbuyomwalendo anamwali ena aja nawonso adabwera nati, ‘Bwana, Bwana, titsekulireni!’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 “Pambuyo pake enawo anabwera nati, ‘Ambuye! Ambuye! Titsekulireni!’

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 25:11
5 Mawu Ofanana  

Pomwepo Ufumu wa Kumwamba udzafanizidwa ndi anamwali khumi, amene anatenga nyali zao, natuluka kukakomana ndi mkwati.


Koma iye anayankha nati, Indetu ndinena kwa inu, sindikudziwani.


Pamene atauka mwini nyumba natseka pakhomo, ndipo inu mudzayamba kuima pabwalo, ndi kugogoda pachitseko, ndi kunena, Ambuye titsegulireni ife; ndipo Iye adzayankha nadzati ndi inu, Sindidziwa inu kumene muchokerako;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa