Mateyu 24:9 - Buku Lopatulika9 Pamenepo adzakuperekani kunsautso, nadzakuphani; ndipo anthu a mitundu yonse adzadana nanu, chifukwa cha dzina langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pamenepo adzakuperekani kunsautso, nadzakuphani; ndipo anthu a mitundu yonse adzadana nanu, chifukwa cha dzina langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Pambuyo pake anthu adzakuperekani kuti mukazunzidwe, kenaka adzakuphani. Anthu a mitundu yonse ya anthu adzadana nanu chifukwa cha Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Pamenepo adzakuperekani kuti mukazunzidwe ndi kuphedwa, ndipo mitundu yonse idzakudani chifukwa cha Ine. Onani mutuwo |