Mateyu 24:48 - Buku Lopatulika48 Koma kapolo woipa akanena mumtima mwake, Mbuye wanga wachedwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Koma kapolo woipa akanena mumtima mwake, Mbuye wanga wachedwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Koma ngati ndi wantchito woipa, mumtima mwake azidzati, ‘Mbuye wanga akuchedwa.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Koma tiyerekeze kuti wantchitoyo ndi woyipa, nati kwa iye yekha, ‘Mbuye wanga akuchedwa kubwera,’ Onani mutuwo |