Mateyu 24:47 - Buku Lopatulika47 Indetu, ndinena kwa inu, kuti adzamkhazika iye woyang'anira zinthu zake zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Indetu, ndinena kwa inu, kuti adzamkhazika iye woyang'anira zinthu zake zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Ndithu ndikunenetsa kuti adzamuika woyang'anira chuma chake chonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Zoonadi, ndikuwuzani kuti adzamuyika kukhala woyangʼanira katundu wake yense. Onani mutuwo |