Mateyu 24:49 - Buku Lopatulika49 nadzayamba kupanda akapolo anzake, nadya ndi kumwa pamodzi ndi oledzera; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 nadzayamba kupanda akapolo anzake, nadya ndi kumwa pamodzi ndi oledzera; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Ndiye adzayamba kumenya antchito anzake, ndiponso kumadya ndi kumamwa pamodzi ndi zidakwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 nayamba kumenya antchito anzake, nadya ndi kumwa ndi zidakwa. Onani mutuwo |