Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 24:40 - Buku Lopatulika

40 Pomwepo adzakhala awiri m'munda; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Pomwepo adzakhala awiri m'munda; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Pa nthaŵi imeneyo anthu aŵiri adzakhala ali m'munda, mmodzi adzamtenga, winayo nkumusiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Amuna awiri adzakhala mʼmunda; wina adzatengedwa ndi wina adzatsala.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 24:40
8 Mawu Ofanana  

ndipo iwo sanadziwe kanthu, kufikira kumene chigumula chinadza, chinapululutsa iwo onse, kotero kudzakhala kufika kwake kwa Mwana wa Munthu.


awiri adzakhala opera pamphero; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.


Pakuti akusiyanitsa iwe ndani? Ndipo uli nacho chiyani chosati wachilandira? Koma ngati wachilandira udzitamanda bwanji, monga ngati sunachilandire?


ndipo sanalekerere dziko lapansi lakale, koma anasunga Nowa mlaliki wa chilungamo, ndi anzake asanu ndi awiri, pakulitengera dziko la osapembedza chigumula;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa