Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 24:41 - Buku Lopatulika

41 awiri adzakhala opera pamphero; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 awiri adzakhala opera pamphero; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 Azimai aŵiri adzakhala akusinja, mmodzi adzamtenga, winayo nkumusiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 Amayi awiri adzakhala akusinja pa mtondo; wina adzatengedwa ndi wina adzatsala.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 24:41
5 Mawu Ofanana  

ndipo ana oyamba a m'dziko la Ejipito adzafa, kuyambira mwana woyamba wa Farao wokhala pa mpando wachifumu wake, kufikira mwana woyamba wa mdzakazi wokhala pa miyala yopera; ndi ana onse oyamba a zoweta.


Tenga mipero, nupere ufa; chotsa chophimba chako, vula chofunda, kwinda m'mwendo, oloka mitsinje.


Pomwepo adzakhala awiri m'munda; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa:


Padzakhala akazi awiri akupera pamodzi, mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.


Munthu asalandire chikole mphero, ngakhale mwanamphero, popeza alandirapo chikole moyo wa munthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa