Mateyu 24:34 - Buku Lopatulika34 Indetu ndinena kwa inu, mbadwo uwu sudzatha kuchoka, kufikira zinthu zonsezi zidzachitidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Indetu ndinena kwa inu, mbadwo uwu sudzatha kuchoka, kufikira zinthu zonsezi zidzachitidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Ndithu ndikunenetsa kuti zonsezi zidzaoneka anthu a mbadwo unoŵa asanamwalire onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Zoonadi, ndikuwuzani kuti mʼbado uwu sudzatha mpaka zinthu zonse zitachitika. Onani mutuwo |