Mateyu 24:33 - Buku Lopatulika33 chomwechonso inu, pamene mudzaona zimenezo, zindikirani kuti Iye ali pafupi, inde pakhomo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 chomwechonso inu, pamene mudzaona zimenezo, zindikirani kuti Iye ali pafupi, inde pakhomo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Momwemonso, mukadzaona zonse ndanena zija, mudzadziŵe kuti Mwana wa Munthu ali pafupi, ali pakhomo penipeni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Momwemonso, pamene mudzaona zinthu zonsezi mudzadziwe kuti ali pafupi pa khomo penipeni. Onani mutuwo |