Mateyu 24:27 - Buku Lopatulika27 Pakuti monga mphezi idzera kum'mawa, nionekera kufikira kumadzulo; kotero kudzakhalanso kufika kwake kwa Mwana wa Munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Pakuti monga mphezi idzera kum'mawa, nionekera kufikira kumadzulo; kotero kudzakhalanso kufika kwake kwa Mwana wa Munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Mwana wa Munthutu kubwera kwake kudzakhala monga muja mphezi imang'animira ndi kuŵala kuchokera kuvuma mpaka kuzambwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Monga momwe mphenzi ingʼanima kuchokera kummawa kupita kumadzulo, momwemonso kudzakhala kubwera kwa Mwana wa Munthu. Onani mutuwo |