Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 24:26 - Buku Lopatulika

26 Onani, Iye ali m'chipululu; musamukeko. Onani, ali m'zipinda; musavomereze.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Onani, ali m'zipinda; musavomereze.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 “Nchifukwa chake, anthu akadzakuuzani kuti, ‘Inu, Khristu ali ku chipululu,’ musadzapiteko. Kapena akadzati, ‘Ali m'kati mwa nyumba,’ musadzakhulupirire.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 “Ndiye ngati wina akuwuzani inu kuti, ‘Uyo ali ku chipululu,’ inu musapiteko; kapena akati, ‘Uyu ali kuno mʼchipinda chamʼkati,’ musakhulupirire.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 24:26
6 Mawu Ofanana  

Mau a wofuula m'chipululu, Konzani njira ya Yehova, lungamitsani m'dziko loti see khwalala la Mulungu wathu.


Chifukwa chake akanena kwa inu,


Pakuti monga mphezi idzera kum'mawa, nionekera kufikira kumadzulo; kotero kudzakhalanso kufika kwake kwa Mwana wa Munthu.


Ndipo masiku aja anadza Yohane Mbatizi, nalalikira m'chipululu cha Yudeya,


Si ndiwe Mwejipito uja kodi, unachita mipanduko kale lija, ndi kutsogolera ambanda aja zikwi zinai kuchipululu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa