Mateyu 24:28 - Buku Lopatulika28 Kumene kulikonse kuli mtembo, miimba idzasonkhanira konko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Kumene kulikonse uli mtembo, miimba idzasonkhanira konko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 “Paja adati, Kulikonse kumene kwafera chinthu, miphamba imasonkhana kumeneko.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Kulikonse kuli chinthu cha kufa, makwangwala adzasonkhanako. Onani mutuwo |