Mateyu 24:19 - Buku Lopatulika19 Koma tsoka ali nalo iwo akukhala ndi pakati, ndi akuyamwitsa ana m'masiku awo! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma tsoka ali nalo iwo akukhala ndi pakati, ndi akuyamwitsa ana m'masiku awo! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ali ndi tsoka azimai amene adzakhale ndi pathupi, ndiponso azimai oyamwitsa ana masiku amenewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Kudzakhala koopsa kwambiri masiku amenewo kwa amayi oyembekezera ndi kwa oyamwitsa! Onani mutuwo |