Mateyu 24:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo pempherani kuti kuthawa kwanu kusakhale pa nyengo yachisanu, kapena pa Sabata; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo pempherani kuti kuthawa kwanu kusakhale pa nyengo yachisanu, kapena pa Sabata; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Pempherani kuti nthaŵi pamene muzidzathaŵa, isadzakhale nyengo yachisanu, kapena pa tsiku la Sabata. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Pempherani kuti kuthawa kwanu kusadzachitike nthawi yozizira kapena pa Sabata. Onani mutuwo |