Mateyu 24:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo chifukwa cha kuchuluka kwa kusaweruzika, chikondano cha anthu aunyinji chidzazilala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo chifukwa cha kuchuluka kwa kusaweruzika, chikondano cha anthu aunyinji chidzazilala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono popeza kuti zoipa zizidzachulukirachulukira, chikondi chizidzacheperachepera pakati pa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Chifukwa cha kuchuluka kwa zoyipa, chikondi cha ambiri chidzazirala, Onani mutuwo |