Mateyu 24:13 - Buku Lopatulika13 Koma iye wakulimbika chilimbikire kufikira kuchimaliziro, yemweyo adzapulumuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma iye wakulimbika chilimbikire kufikira kuchimaliziro, yemweyo adzapulumuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma yemwe adzalimbikire mpaka potsiriza, ameneyo ndiye adzapulumuke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 koma wopirira kufikira chimaliziro adzapulumuka. Onani mutuwo |