Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 24:13 - Buku Lopatulika

13 Koma iye wakulimbika chilimbikire kufikira kuchimaliziro, yemweyo adzapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Koma iye wakulimbika chilimbikire kufikira kuchimaliziro, yemweyo adzapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Koma yemwe adzalimbikire mpaka potsiriza, ameneyo ndiye adzapulumuke.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 koma wopirira kufikira chimaliziro adzapulumuka.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 24:13
12 Mawu Ofanana  

Ndipo adzada inu anthu onse chifukwa cha dzina langa; koma iye wakupirira kufikira chimaliziro, iyeyu adzapulumutsidwa.


Ndipo chifukwa cha kuchuluka kwa kusaweruzika, chikondano cha anthu aunyinji chidzazilala.


Koma inu mudzayamba kumva za nkhondo, ndi mbiri za nkhondo; onani, musadere nkhawa; pakuti kuyenera kuti izi zioneke; koma chitsiriziro sichinafike.


Ndipo adzada inu anthu onse chifukwa cha dzina langa: koma iye wakupirira kufikira chimaliziro, yemweyo adzapulumutsidwa.


Mudzakhala nao moyo wanu m'chipiriro.


Ndipo zija za m'nthaka yokoma, ndiwo amene anamva mau nawasunga mu mtima woona ndi wabwino, nabala zipatso ndi kupirira.


kwa iwo amene afunafuna ulemerero ndi ulemu ndi chisaonongeko, mwa kupirira pa ntchito zabwino, adzabwezera moyo wosatha;


amenenso adzakukhazikitsani inu kufikira chimaliziro, kuti mukhale opanda chifukwa m'tsiku la Ambuye wathu Yesu Khristu.


Koma ife si ndife a iwo akubwerera kulowa chitayiko; koma a iwo a chikhulupiriro cha ku chipulumutso cha moyo.


pakuti takhala ife olandirana ndi Khristu, ngatitu tigwiritsa chiyambi cha kutama kwathu kuchigwira kufikira chitsiriziro;


koma Khristu monga mwana, wosunga nyumba yake; ndife nyumba yake, ngati tigwiritsa kulimbika mtima ndi kudzitamandira kwa chiyembekezocho, kuchigwira kufikira chitsiriziro.


Usaope zimene uti udzamve kuwawa; taona, mdierekezi adzaponya ena a inu m'nyumba yandende, kuti mukayesedwe; ndipo mudzakhala nacho chisautso masiku khumi. Khala wokhulupirika kufikira imfa, ndipo ndidzakupatsa iwe korona wa moyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa