Mateyu 23:8 - Buku Lopatulika8 Koma inu musatchedwa Rabi; pakuti Mphunzitsi wanu ali mmodzi, ndipo inu nonse muli abale. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Koma inu musatchedwa Rabi; pakuti Mphunzitsi wanu ali mmodzi, ndipo inu nonse muli abale. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Koma inuyo anthu asati azikutchulani aphunzitsi, pakuti muli ndi Mphunzitsi mmodzi yekha, ndipo nonsenu muli pa chibale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Koma inu simuyenera kutchulidwa ‘Aphunzitsi,’ popeza muli naye Mbuye mmodzi ndipo inu nonse ndinu abale. Onani mutuwo |