Mateyu 23:7 - Buku Lopatulika7 ndi kulonjeredwa m'misika, ndi kutchedwa ndi anthu, Rabi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 ndi kulonjeredwa m'misika, ndi kutchedwa ndi anthu, Rabi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Amakondanso kuti anthu aziŵalonjera mwaulemu pa misika, ndipo kuti aziŵatchula aphunzitsi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Amakondwera ndi kupatsidwa moni mʼmisika ndi kutchulidwa kuti ‘Aphunzitsi.’ Onani mutuwo |