Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 23:6 - Buku Lopatulika

6 nakonda malo a ulemu pamaphwando, ndi mipando ya ulemu m'masunagoge,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 nakonda malo a ulemu pamaphwando, ndi mipando ya ulemu m'masunagoge,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Amakonda malo olemekezeka pa maphwando ndiponso mipando yaulemu kwambiri ku nyumba zamapemphero.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Amakonda malo aulemu pa maphwando ndi malo ofunika kwambiri mʼmasunagoge.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 23:6
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anati kwa iye, Ufuna chiyani? Iye ananena, Lamulirani kuti ana anga awiri amenewa adzakhale, wina ku dzanja lanu lamanja, ndi wina kulamanzere, mu ufumu wanu.


M'chikondano cha anzanu wina ndi mnzake mukondane ndi chikondi chenicheni; mutsogolerane ndi kuchitira wina mnzake ulemu;


Ndalemba kanthu kwa Mpingo; komatu Diotrefe uja, wofuna kukhala wamkulu wa iwo, satilandira ife.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa