Mateyu 23:26 - Buku Lopatulika26 Mfarisi iwe wakhungu, yambawatsuka m'kati mwa chikho ndi mbale, kuti kunja kwake kukhalenso koyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Mfarisi iwe wakhungu, yambotsuka m'kati mwa chikho ndi mbale, kuti kunja kwake kukhalenso koyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Afarisi akhungu inu, yambani mwatsuka m'kati mwa chikho, ndipo kunja kwakenso kudzayera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Afarisi akhungu! Poyamba tsukani mʼkati mwa chikho ndi mbale, ndipo kunja kwake kudzakhalanso koyera. Onani mutuwo |