Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 23:25 - Buku Lopatulika

25 Tsoka inu, alembi ndi Afarisi, onyenga! Chifukwa mutsuka kunja kwake kwa chikho ndi mbale, koma m'katimo iwo adzala ndi kulanda ndi kusadziletsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Tsoka inu, alembi ndi Afarisi, onyenga! Chifukwa mutsuka kunja kwake kwa chikho ndi mbale, koma m'katimo iwo adzala ndi kulanda ndi kusadziletsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 “Muli ndi tsoka, inu aphunzitsi a Malamulo ndi Afarisi, anthu achiphamaso! Mumatsuka kunja kwa chikho ndi kwa mbale koma m'kati mwake m'modzaza ndi nzeru zakuba, ndi zaumbombo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 “Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi achiphamaso! Mumayeretsa kunja kwa chikho ndi mbale, koma mʼkatimo mwadzaza ndi dyera ndi kusadziretsa.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 23:25
6 Mawu Ofanana  

Ndipo iye, atampangira amake, anati, Ndipatseni ine kuno m'mbale mutu wa Yohane Mbatizi.


ameneyo, pokhala nao maonekedwe a Mulungu, sanachiyese cholanda kukhala wofana ndi Mulungu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa