Mateyu 22:5 - Buku Lopatulika5 Koma iwo ananyalanyaza, nachoka, wina kumunda wake, wina kumalonda ake: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma iwo ananyalanyaza, nachoka, wina kumunda wake, wina kumalonda ake: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma oitanidwawo sadalabadireko, adangopita ku zao: wina kumunda kwake, wina ku ntchito yake yamalonda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Koma iwo sanalabadire ndipo anachoka; wina anapita ku munda wake ndi wina ku malonda ake. Onani mutuwo |