Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 22:6 - Buku Lopatulika

6 ndipo otsala anagwira akapolo ake, nawachitira chipongwe, nawapha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 ndipo otsala anagwira akapolo ake, nawachitira chipongwe, nawapha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Enawo adagwira antchito a mfumu aja naŵazunza, nkuŵapha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Ndipo otsalawo anagwira antchito ake, nawazunza ndi kuwapha.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 22:6
16 Mawu Ofanana  

Koma iwo ananyalanyaza, nachoka, wina kumunda wake, wina kumalonda ake:


Koma mfumu inakwiya; nituma asilikali ake napululutsa ambanda aja, nitentha mzinda wao.


Pakuti adzampereka kwa amitundu, nadzamseka, nadzamchitira chipongwe, nadzamthira malovu;


Ndipo Saulo analikuvomerezana nao pa imfa yake. Ndipo tsikulo kunayamba kuzunza kwakukulu pa Mpingo unali mu Yerusalemu; ndipo anabalalitsidwa onse m'maiko a Yudeya ndi Samariya, koma osati atumwi ai.


Kumbukirani am'nsinga, monga am'nsinga anzao; ochitidwa zoipa, monga ngati inunso adatero nanu m'thupi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa