Mateyu 22:6 - Buku Lopatulika6 ndipo otsala anagwira akapolo ake, nawachitira chipongwe, nawapha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndipo otsala anagwira akapolo ake, nawachitira chipongwe, nawapha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Enawo adagwira antchito a mfumu aja naŵazunza, nkuŵapha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo otsalawo anagwira antchito ake, nawazunza ndi kuwapha. Onani mutuwo |