Mateyu 22:45 - Buku Lopatulika45 Chifukwa chake ngati Davide amtchula Iye Ambuye, ali mwana wake bwanji? Ndipo panalibe mmodzi anatha kumyankha mau. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Chifukwa chake ngati Davide amtchula Iye Ambuye, ali mwana wake bwanji? Ndipo panalibe mmodzi anatha kumyankha mau. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 “Ngati Davide akutchula Mpulumutsi wolonjezedwa uja kuti Mbuye wake, angakhale mwana wakenso bwanji?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Ngati tsono Davide amamutchula ‘Ambuye,’ zingatheke bwanji kukhala mwana wake?” Onani mutuwo |