Mateyu 22:44 - Buku Lopatulika44 Ambuye ananena kwa Ambuye wanga, ukhale padzanja lamanja langa, kufikira Ine ndidzaika adani ako pansi pa mapazi ako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Ambuye ananena kwa Ambuye wanga, ukhale pa dzanja lamanja langa, kufikira Ine ndidzaika adani ako pansi pa mapazi ako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 “ ‘Chauta adauza Mbuye wanga kuti, Khala ku dzanja langa lamanja, mpaka nditasandutsa adani ako kuti akhale ngati chopondapo mapazi ako.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 “Ambuye anati kwa Ambuye wanga: ‘Khala pa dzanja langa lamanja mpaka ndiyike adani ako pansi pa mapazi ako.’ Onani mutuwo |