Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 22:34 - Buku Lopatulika

34 Koma Afarisi, pakumva kuti Iye anatontholetsa Asaduki, anasonkhana.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Koma Afarisi, pakumva kuti Iye anatontholetsa Asaduki, anasonkhana.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Afarisi atamva kuti Yesu adatsutsa Asaduki, adasonkhana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Pakumva kuti Yesu anawakhalitsa chete Asaduki, Afarisi anasonkhana pamodzi.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 22:34
10 Mawu Ofanana  

Ndipo Afarisi anatuluka, nakhala upo womchitira Iye mwa kumuononga.


Ndipo iye pakuona ambiri a Afarisi ndi a Asaduki akudza ku ubatizo wake, anati kwa iwo, Obadwa a njoka inu, ndani anakulangizani kuthawa mkwiyo ulinkudza?


Ndipo taonani, wachilamulo wina anaimirira namuyesa Iye, nanena, Mphunzitsi, ndidzalowa moyo wosatha ndi kuchita chiyani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa