Mateyu 22:33 - Buku Lopatulika33 Ndipo pamene makamu a anthu anamva, anazizwa ndi chiphunzitso chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Ndipo pamene makamu a anthu anamva, anazizwa ndi chiphunzitso chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Pamene anthu ochuluka aja amene anali pamenepo adamva zimenezi, adadabwa kwambiri ndi zophunzitsa zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Magulu a anthu atamva zimenezi, anazizwa ndi chiphunzitso chake. Onani mutuwo |