Mateyu 22:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo mmodzi wa iwo, mphunzitsi wa malamulo, anamfunsa ndi kumuyesa Iye, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo mmodzi wa iwo, mphunzitsi wa chilamulo, anamfunsa ndi kumuyesa Iye, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Tsono mmodzi mwa iwo, katswiri wa Malamulo, adafunsa Yesu funso kuti amutape m'kamwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Mmodzi wa iwo, katswiri wa malamulo anamuyesa Iye ndi funso ndipo anati, Onani mutuwo |